Mateyu 8:3 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 3 Pamenepo Yesu anatambasula dzanja lake n’kumukhudza, ndipo anati: “Ndikufuna. Khala woyera.”+ Nthawi yomweyo khate lakelo linatha.+ Maliko 1:42 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 42 Nthawi yomweyo khate lakelo linatha, ndipo anakhala woyera.+
3 Pamenepo Yesu anatambasula dzanja lake n’kumukhudza, ndipo anati: “Ndikufuna. Khala woyera.”+ Nthawi yomweyo khate lakelo linatha.+