Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mateyu 10:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 “Mukalowa mumzinda kapena m’mudzi uliwonse, fufuzani mmenemo yemwe ali woyenerera, ndipo mukhalebe momwemo kufikira nthawi yochoka.+

  • Maliko 6:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Komanso anawauza kuti: “Mukafika pakhomo lililonse,+ khalani pamenepo mpaka nthawi yochoka kumeneko itakwana.+

  • Luka 10:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Mukafika panyumba, choyamba muzinena kuti, ‘Mtendere ukhale panyumba pano.’+

  • Luka 10:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Choncho khalani m’nyumba yamtendereyo.+ Muzidya ndi kumwa zimene angakupatseni,+ chifukwa wantchito ayenera kulandira malipiro ake.+ Musamachoke kumene mwafikirako n’kupita kunyumba zina.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena