Mateyu 12:30 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 30 Amene sali kumbali yanga ndi wotsutsana ndi ine, ndipo amene sagwira limodzi ndi ine ntchito yosonkhanitsa anthu kwa ine amawabalalitsa.+ Luka 11:23 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 23 Amene sali kumbali yanga akutsutsana ndi ine, ndipo amene sasonkhanitsa anthu pamodzi ndi ine amawabalalitsa.+ 1 Akorinto 12:3 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 3 Choncho ndikufuna mudziwe kuti palibe wolankhula mwa mzimu wa Mulungu amene anganene kuti: “Yesu ndi wotembereredwa!”+ Palibenso amene anganene popanda mzimu woyera kuti: “Yesu ndiye Ambuye!”+ Afilipi 1:18 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 18 Akatero ndiye kuti achita chiyani? Palibe! Mulimonse mmene zingakhalire, kaya ndi mwachiphamaso+ kapena m’choonadi, Khristu akufalitsidwabe.+ Choncho ine ndikukondwera. Ndipotu ndipitiriza kukondwera,
30 Amene sali kumbali yanga ndi wotsutsana ndi ine, ndipo amene sagwira limodzi ndi ine ntchito yosonkhanitsa anthu kwa ine amawabalalitsa.+
23 Amene sali kumbali yanga akutsutsana ndi ine, ndipo amene sasonkhanitsa anthu pamodzi ndi ine amawabalalitsa.+
3 Choncho ndikufuna mudziwe kuti palibe wolankhula mwa mzimu wa Mulungu amene anganene kuti: “Yesu ndi wotembereredwa!”+ Palibenso amene anganene popanda mzimu woyera kuti: “Yesu ndiye Ambuye!”+
18 Akatero ndiye kuti achita chiyani? Palibe! Mulimonse mmene zingakhalire, kaya ndi mwachiphamaso+ kapena m’choonadi, Khristu akufalitsidwabe.+ Choncho ine ndikukondwera. Ndipotu ndipitiriza kukondwera,