Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mateyu 27:62
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 62 Tsiku lotsatira, pambuyo pa Tsiku Lokonzekera,+ ansembe aakulu ndi Afarisi anasonkhana pamaso pa Pilato,

  • Yohane 19:31
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 31 Popeza linali Tsiku Lokonzekera,+ Ayudawo sanafune kuti mitembo ikhalebe+ pamitengo yozunzikirapo tsiku la Sabata, (pakuti Sabata la tsiku limeneli linali lalikulu,)+ choncho anapempha Pilato kuti opachikidwawo awathyole miyendo ndi kutsitsa mitemboyo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena