Luka 12:51 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 51 Kodi mukuganiza kuti ndinabweretsa mtendere padziko lapansi? Ayi ndithu, koma ndinabwera kudzagawanitsa anthu.+ Yohane 7:12 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 12 Ndipo panali manong’onong’o ambiri onena za iye m’khamu lonse la anthulo.+ Ena anali kunena kuti: “Amene uja ndi munthu wabwino.” Ndipo ena anali kunena kuti: “Ayi si munthu wabwino amene uja, iye akusocheretsa anthu ambiri.” Yohane 9:16 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 16 Ena mwa Afarisiwo anayamba kunena kuti: “Munthu ameneyu si wochokera kwa Mulungu, chifukwa sasunga Sabata.”+ Ena anayamba kunena kuti: “Koma munthu wochimwa angachite bwanji zizindikiro+ zoterezi?” Choncho panakhala kugawanika+ pakati pawo.
51 Kodi mukuganiza kuti ndinabweretsa mtendere padziko lapansi? Ayi ndithu, koma ndinabwera kudzagawanitsa anthu.+
12 Ndipo panali manong’onong’o ambiri onena za iye m’khamu lonse la anthulo.+ Ena anali kunena kuti: “Amene uja ndi munthu wabwino.” Ndipo ena anali kunena kuti: “Ayi si munthu wabwino amene uja, iye akusocheretsa anthu ambiri.”
16 Ena mwa Afarisiwo anayamba kunena kuti: “Munthu ameneyu si wochokera kwa Mulungu, chifukwa sasunga Sabata.”+ Ena anayamba kunena kuti: “Koma munthu wochimwa angachite bwanji zizindikiro+ zoterezi?” Choncho panakhala kugawanika+ pakati pawo.