Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mika 7:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Pakuti mwana wamwamuna akunyoza bambo ake. Mwana wamkazi akuukira mayi ake+ ndipo mkazi wokwatiwa akuukira apongozi ake aakazi.+ Adani ake a munthu ndi anthu a m’banja lake.+

  • Mateyu 10:34
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 34 Musaganize kuti ndinabweretsa mtendere padziko lapansi, sindinabweretse mtendere+ koma lupanga.

  • Yohane 7:43
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 43 Choncho khamu la anthulo linagawanika pa nkhani ya iye.+

  • Yohane 9:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Ena mwa Afarisiwo anayamba kunena kuti: “Munthu ameneyu si wochokera kwa Mulungu, chifukwa sasunga Sabata.”+ Ena anayamba kunena kuti: “Koma munthu wochimwa angachite bwanji zizindikiro+ zoterezi?” Choncho panakhala kugawanika+ pakati pawo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena