Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mateyu 10:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Chenjerani ndi anthu,+ pakuti adzakuperekani kumakhoti aang’ono,+ ndipo adzakukwapulani+ m’masunagoge awo.+

  • Maliko 13:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 “Koma inu khalani wochenjera. Anthu adzakuperekani kumakhoti aang’ono,+ ndipo adzakukwapulani m’masunagoge+ ndi kukuimikani pamaso pa abwanamkubwa ndi mafumu chifukwa cha ine, kuti ukhale umboni kwa iwo.+

  • Luka 20:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Koma nyengo ya zipatso itakwana anatumiza kapolo+ wake kwa alimiwo,+ kuti akamupatseko zina mwa zipatso za m’munda wa mpesawo.+ Komano alimiwo anamumenya ndi kumubweza chimanjamanja.+

  • Machitidwe 22:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Ndipo ine ndinanena kuti, ‘Ambuye, iwowo akudziwa bwino kwambiri kuti anthu amene anali kukukhulupirirani ndinali kuwaponya m’ndende+ ndi kuwakwapula m’sunagoge ndi sunagoge.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena