Deuteronomo 3:28 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 28 Uike Yoswa kukhala mtsogoleri+ ndipo umulimbikitse ndi kumulimbitsa, chifukwa ndiye adzawolotsa+ anthuwa ndi kuwachititsa kulandira dziko limene ulionelo kukhala cholowa chawo.’+ Deuteronomo 31:3 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 3 Yehova Mulungu wanu akuwoloka patsogolo panu kuti akutsogolereni.+ Iye ndiye adzawononga mitundu imeneyi pamaso panu, ndipo inu mudzaipitikitse.+ Yoswa ndiye adzakutsogolerani ndi kukuwolotsani,+ monga mmene Yehova wanenera. Yoswa 3:14 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 14 Ndipo zimenezi zinachitikadi. Anthuwo anachotsa mahema awo, n’kunyamuka. Anayandikira Yorodano kuti awoloke, ndipo ansembe onyamula likasa+ la pangano anali patsogolo pawo.
28 Uike Yoswa kukhala mtsogoleri+ ndipo umulimbikitse ndi kumulimbitsa, chifukwa ndiye adzawolotsa+ anthuwa ndi kuwachititsa kulandira dziko limene ulionelo kukhala cholowa chawo.’+
3 Yehova Mulungu wanu akuwoloka patsogolo panu kuti akutsogolereni.+ Iye ndiye adzawononga mitundu imeneyi pamaso panu, ndipo inu mudzaipitikitse.+ Yoswa ndiye adzakutsogolerani ndi kukuwolotsani,+ monga mmene Yehova wanenera.
14 Ndipo zimenezi zinachitikadi. Anthuwo anachotsa mahema awo, n’kunyamuka. Anayandikira Yorodano kuti awoloke, ndipo ansembe onyamula likasa+ la pangano anali patsogolo pawo.