-
Aroma 16:26Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
26 Koma tsopano chinsinsi chopatulika chimenechi chaonetsedwa+ ndipo chadziwika pakati pa mitundu yonse ya anthu kudzera m’malemba aulosi. Zimenezi n’zogwirizana ndi lamulo la Mulungu wokhalako kwamuyaya. Cholinga chake n’chakuti anthu a mitundu yonse amukhulupirire ndi kumumvera mwa chikhulupiriro.+
-