Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Aroma 6:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Ndikulankhulatu monga munthu chifukwa cha kufooka kwa matupi anu.+ Pakuti mmene munaperekera ziwalo zanu+ kuti zikhale akapolo a zonyansa+ ndiponso akapolo a kusamvera malamulo ndi cholinga chakuti muzichita zinthu zophwanya malamulo, perekaninso ziwalo zanu kuti zikhale akapolo a chilungamo kuti muzichita ntchito za chiyero.+

  • 1 Atesalonika 4:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Akufunanso kuti aliyense wa inu akhale woyera mwa kudziwa kulamulira thupi lake+ m’njira yoyera+ kuti mukhale olemekezeka pamaso pa Mulungu,

  • Aheberi 10:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Mwa “chifuniro”+ chimenecho, tayeretsedwa+ kudzera m’thupi la Yesu Khristu loperekedwa nsembe+ kamodzi+ kokha.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena