Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Atesalonika 4
  • Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

1 Atesalonika 4:1

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Akl 1:10; 1Pe 2:12
  • +Afi 1:27

1 Atesalonika 4:2

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +1Ti 6:13

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    10/1/1986, ptsa. 23-24

1 Atesalonika 4:3

Mawu a M'munsi

  • *

    Onani Zakumapeto 7.

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Yoh 17:19; Aef 5:26; 2At 2:13; 1Pe 1:16
  • +1Ak 6:15; Aef 5:3

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Mungakhale Ndi Moyo Mpaka Kalekale, lesson 41

    Nsanja ya Olonda,

    6/1/2012, tsa. 21

    7/15/1997, tsa. 18

    11/1/1989, ptsa. 12-13

    10/1/1986, tsa. 23

1 Atesalonika 4:4

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Akl 3:5; 2Ti 2:22
  • +Aro 6:19; 2Ti 2:21

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Galamukani!,

    10/8/2003, tsa. 31

    Nsanja ya Olonda,

    10/1/1986, tsa. 23

1 Atesalonika 4:5

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +1Ak 6:18; Aef 5:5
  • +1Ak 5:10; Aef 4:17
  • +Sl 79:6; 1Pe 4:3

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Galamukani!,

    9/2013, tsa. 5

    Nsanja ya Olonda,

    6/1/2012, tsa. 21

    10/1/1986, tsa. 23

1 Atesalonika 4:6

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 5:21; 1Ak 6:8; 7:2
  • +Sl 94:1; 2At 1:8
  • +Mac 20:20; 28:23

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Galamukani!,

    11/2006, tsa. 14

    5/8/2000, ptsa. 29-30

    Nsanja ya Olonda,

    6/15/2002, ptsa. 20-21

    1/15/2001, tsa. 7

    7/15/1997, tsa. 18

    11/15/1989, tsa. 31

    Mtendere Weniweni, ptsa. 144-146

1 Atesalonika 4:7

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Le 11:44; 1Ak 1:2; Ahe 12:14; 1Pe 1:15

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda (Yophunzira),

    6/2023, ptsa. 12-13

    Nsanja ya Olonda,

    6/1/2012, tsa. 21

1 Atesalonika 4:8

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Lu 10:16
  • +1Ak 6:19
  • +Eze 37:14; 1Yo 3:24

1 Atesalonika 4:9

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Yoh 13:34, 35; Aro 12:10
  • +Yes 54:13; Yoh 6:45
  • +1Pe 1:22; 1Yo 4:21

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    10/1/1986, ptsa. 23-24

1 Atesalonika 4:10

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    2/1/2003, ptsa. 13-14

    10/1/1986, ptsa. 23-24

1 Atesalonika 4:11

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +2At 3:12
  • +Aro 12:11; 1Pe 4:15
  • +1Ak 4:12; Aef 4:28; 2At 3:10; 1Ti 5:8

1 Atesalonika 4:12

Mawu a M'munsi

  • *

    Amenewa ndi anthu amene sali mumpingo wachikhristu.

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Aro 13:13
  • +Aro 12:17; 2Ak 8:21
  • +Yak 1:4

1 Atesalonika 4:13

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Yoh 11:11; Mac 7:60; 1Ak 15:6
  • +1Ak 15:32; Aef 2:12

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Galamukani!,

    7/8/2001, ptsa. 30-31

    5/8/1994, tsa. 31

    2/8/1988, tsa. 11

    Nsanja ya Olonda,

    10/15/1994, tsa. 32

    10/1/1986, ptsa. 24-25

1 Atesalonika 4:14

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Aro 14:9; 1Ak 15:4
  • +1Ak 15:23; Afi 3:21; 2At 2:1; Chv 20:4

1 Atesalonika 4:15

Mawu a M'munsi

  • *

    Onani Zakumapeto 8.

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +1At 2:13; 1Yo 4:2
  • +Mt 24:30; 1Ak 15:51

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    1/1/2007, tsa. 28

    1/15/1993, tsa. 5

    Mapeto a Chivumbulutso, ptsa. 103-104

1 Atesalonika 4:16

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Mac 1:11
  • +Yuda 9
  • +Mt 24:31
  • +1Ak 15:52

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Kuyankha Mafunso a M’Baibulo,

    Nsanja ya Olonda (Yogawira),

    No. 5 2017, tsa. 5

    Nsanja ya Olonda,

    1/1/2007, tsa. 28

    1/15/1993, ptsa. 5-6

    10/1/1986, ptsa. 25-26

    Mapeto a Chivumbulutso, ptsa. 103-104, 180-181

    Galamukani!,

    2/8/2002, tsa. 31

    Kukambitsirana, ptsa. 212-218, 432

1 Atesalonika 4:17

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +2Ti 4:8
  • +Mac 1:9; 2Ak 5:8; Afi 1:23
  • +Mt 26:64
  • +Yoh 12:26; 17:24; 2At 2:1
  • +Yoh 14:3; Chv 20:6

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    7/15/2015, ptsa. 17-19

    9/15/2008, tsa. 29

    1/1/2007, tsa. 28

    1/15/1993, ptsa. 4-6

    10/1/1986, tsa. 26

    Mapeto a Chivumbulutso, ptsa. 103-104, 211

    Kukambitsirana, ptsa. 212-218

1 Atesalonika 4:18

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    10/1/1986, ptsa. 10-26

Mabaibulo Ena

Dinani pa nambala ya vesi kuti muone mavesi a m'Baibulo lina ofanana ndi vesilo.

Malemba Ena

1 Ates. 4:1Akl 1:10; 1Pe 2:12
1 Ates. 4:1Afi 1:27
1 Ates. 4:21Ti 6:13
1 Ates. 4:3Yoh 17:19; Aef 5:26; 2At 2:13; 1Pe 1:16
1 Ates. 4:31Ak 6:15; Aef 5:3
1 Ates. 4:4Akl 3:5; 2Ti 2:22
1 Ates. 4:4Aro 6:19; 2Ti 2:21
1 Ates. 4:51Ak 6:18; Aef 5:5
1 Ates. 4:51Ak 5:10; Aef 4:17
1 Ates. 4:5Sl 79:6; 1Pe 4:3
1 Ates. 4:6De 5:21; 1Ak 6:8; 7:2
1 Ates. 4:6Sl 94:1; 2At 1:8
1 Ates. 4:6Mac 20:20; 28:23
1 Ates. 4:7Le 11:44; 1Ak 1:2; Ahe 12:14; 1Pe 1:15
1 Ates. 4:8Lu 10:16
1 Ates. 4:81Ak 6:19
1 Ates. 4:8Eze 37:14; 1Yo 3:24
1 Ates. 4:9Yoh 13:34, 35; Aro 12:10
1 Ates. 4:9Yes 54:13; Yoh 6:45
1 Ates. 4:91Pe 1:22; 1Yo 4:21
1 Ates. 4:112At 3:12
1 Ates. 4:11Aro 12:11; 1Pe 4:15
1 Ates. 4:111Ak 4:12; Aef 4:28; 2At 3:10; 1Ti 5:8
1 Ates. 4:12Aro 13:13
1 Ates. 4:12Aro 12:17; 2Ak 8:21
1 Ates. 4:12Yak 1:4
1 Ates. 4:13Yoh 11:11; Mac 7:60; 1Ak 15:6
1 Ates. 4:131Ak 15:32; Aef 2:12
1 Ates. 4:14Aro 14:9; 1Ak 15:4
1 Ates. 4:141Ak 15:23; Afi 3:21; 2At 2:1; Chv 20:4
1 Ates. 4:151At 2:13; 1Yo 4:2
1 Ates. 4:15Mt 24:30; 1Ak 15:51
1 Ates. 4:16Mac 1:11
1 Ates. 4:16Yuda 9
1 Ates. 4:16Mt 24:31
1 Ates. 4:161Ak 15:52
1 Ates. 4:172Ti 4:8
1 Ates. 4:17Mac 1:9; 2Ak 5:8; Afi 1:23
1 Ates. 4:17Mt 26:64
1 Ates. 4:17Yoh 12:26; 17:24; 2At 2:1
1 Ates. 4:17Yoh 14:3; Chv 20:6
  • Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Werengani mu Baibulo la Dziko Latsopano (nwt)
  • 1
  • 2
  • 3
  • 4
  • 5
  • 6
  • 7
  • 8
  • 9
  • 10
  • 11
  • 12
  • 13
  • 14
  • 15
  • 16
  • 17
  • 18
Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
1 Atesalonika 4:1-18

1 Atesalonika

4 Pomalizira abale, tinakulangizani za mmene muyenera kuyendera+ ndi mmene muyenera kukondweretsera Mulungu, ndipo mukuchitadi zimenezo. Tsopano tikufuna kukudandaulirani ndi kukupemphani m’dzina la Ambuye Yesu kuti mupitirize kuchita zimenezi mowonjezereka.+ 2 Pakuti mukudziwa malamulo+ amene tinakupatsani mwa ulamuliro wa Ambuye Yesu.

3 Mulungu akufuna kuti mukhale oyera+ mwa kupewa dama.*+ 4 Akufunanso kuti aliyense wa inu akhale woyera mwa kudziwa kulamulira thupi lake+ m’njira yoyera+ kuti mukhale olemekezeka pamaso pa Mulungu, 5 osati mwa chilakolako chosalamulirika cha kugonana,+ ngati chimene anthu a mitundu ina+ osadziwa Mulungu+ ali nacho. 6 Koma akufuna kuti pasapezeke wina wopweteka m’bale wake kapena womuphwanyira ufulu wake pa nkhani imeneyi,+ chifukwa Yehova adzalanga anthu onse ochita zimenezi,+ monga mmene tinakuuzirani kale ndi kukufotokozerani momveka bwino.+ 7 Pakuti Mulungu sanatiitane mwa kulekerera zodetsa, koma kuti tikhale oyera.+ 8 Choncho munthu wonyalanyaza+ chiphunzitso chimenechi sakunyalanyaza munthu, koma Mulungu+ amene amaika mzimu wake woyera+ mwa inu.

9 Koma za kukonda abale,+ n’zosafunika kuti tizichita kukulemberani pakuti inu nomwe, Mulungu amakuphunzitsani+ kukondana.+ 10 Ndipo inu mukuchitadi zimenezi kwa abale onse ku Makedoniya konse. Koma tikukudandaulirani abale kuti mupitirize kutero mowonjezereka. 11 Ndiponso muyesetse kukhala mwamtendere,+ kusalowerera mu nkhani za eni,+ ndi kugwira ntchito ndi manja anu+ monga mmene tinakulamulirani. 12 Mutero kuti muziyenda moyenerera+ pamaso pa anthu akunja*+ ndiponso kuti mukhale osasowa kanthu.+

13 Komanso abale, sitikufuna kuti mukhale osadziwa za amene akugona+ mu imfa, kuti musachite chisoni mofanana ndi mmene onse opanda chiyembekezo+ amachitira. 14 Pakuti ngati timakhulupirira kuti Yesu anafa ndi kuukanso,+ ndiye kuti amenenso agona mu imfa kudzera mwa Yesu, Mulungu adzawasonkhanitsa kuti akhale naye limodzi.+ 15 Pakuti tikukuuzani izi mogwirizana ndi mawu a Yehova+ kuti, ife amoyofe amene tidzakhalapo pa nthawi ya kukhalapo* kwa Ambuye,+ sitidzakhala patsogolo pa amene agona mu imfa. 16 Chifukwa Ambuye mwini adzatsika kumwamba,+ ndi mfuu yolamula ya mawu a mkulu wa angelo,+ ndi lipenga+ la Mulungu. Ndipo amene anafa mwa Khristu adzauka choyamba.+ 17 Pambuyo pake ife amoyo otsalafe, limodzi ndi iwowo,+ tidzatengedwa+ m’mitambo+ kukakumana+ ndi Ambuye m’mlengalenga, ndipo tizikakhala ndi Ambuye nthawi zonse.+ 18 Choncho, muzilimbikitsana ndi mawu amenewa.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena