Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Machitidwe 1:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Atatsiriza kunena zimenezi, Mulungu anamunyamula kupita m’mlengalenga iwo akuonerera,+ ndipo mtambo unamuphimba moti sanathenso kumuona.+

  • 2 Akorinto 5:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Koma tikulimba mtima ndipo ndife okondwa kukakhala ndi Ambuye, m’malo mokhala m’thupi linoli.+

  • Afilipi 1:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Ndapanikizika ndi zinthu ziwirizi,+ koma chimene ndikufuna ndicho kumasuka ndi kukhala ndi Khristu.+ Pakuti kunena zoona, chimenechi ndiye chabwino kwambiri.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena