Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Atesalonika 3
  • Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

1 Atesalonika 3:1

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Mac 17:15

1 Atesalonika 3:2

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Mac 16:1; Aro 16:21; 1Ak 16:10
  • +Mt 24:14; 2At 1:8; Chv 14:6

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    5/15/2009, tsa. 14

    10/1/1986, ptsa. 10-23

1 Atesalonika 3:3

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Mac 14:22; Aef 3:13
  • +1Ak 4:9; 1Pe 2:21

1 Atesalonika 3:4

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +2At 2:5
  • +Mac 20:23
  • +1At 2:14

1 Atesalonika 3:5

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +1At 3:2
  • +Mt 4:3; 1Ak 7:5; 2Ak 11:3
  • +1Ak 15:58; Aga 4:11; Afi 2:16

1 Atesalonika 3:6

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Mac 18:5
  • +Aro 13:8; Yak 2:8; 1Pe 1:22
  • +Afi 1:8

1 Atesalonika 3:7

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +2At 1:4
  • +2Ak 7:6

1 Atesalonika 3:8

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Aro 11:20; 1Ak 15:1; Afi 4:1

1 Atesalonika 3:9

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Afi 2:2

1 Atesalonika 3:10

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +2Ti 1:3
  • +2At 1:3; Yuda 20

1 Atesalonika 3:11

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +2At 2:16

1 Atesalonika 3:12

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +2At 1:3
  • +1At 4:9; 2Pe 1:7

1 Atesalonika 3:13

Mawu a M'munsi

  • *

    Onani Zakumapeto 8.

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +1Ak 1:8; Afi 1:10
  • +Yak 5:8; 1Yo 2:28
  • +1At 2:19; 5:23; 2At 2:1

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    10/1/1986, tsa. 23

Mabaibulo Ena

Dinani pa nambala ya vesi kuti muone mavesi a m'Baibulo lina ofanana ndi vesilo.

Malemba Ena

1 Ates. 3:1Mac 17:15
1 Ates. 3:2Mac 16:1; Aro 16:21; 1Ak 16:10
1 Ates. 3:2Mt 24:14; 2At 1:8; Chv 14:6
1 Ates. 3:3Mac 14:22; Aef 3:13
1 Ates. 3:31Ak 4:9; 1Pe 2:21
1 Ates. 3:42At 2:5
1 Ates. 3:4Mac 20:23
1 Ates. 3:41At 2:14
1 Ates. 3:51At 3:2
1 Ates. 3:5Mt 4:3; 1Ak 7:5; 2Ak 11:3
1 Ates. 3:51Ak 15:58; Aga 4:11; Afi 2:16
1 Ates. 3:6Mac 18:5
1 Ates. 3:6Aro 13:8; Yak 2:8; 1Pe 1:22
1 Ates. 3:6Afi 1:8
1 Ates. 3:72At 1:4
1 Ates. 3:72Ak 7:6
1 Ates. 3:8Aro 11:20; 1Ak 15:1; Afi 4:1
1 Ates. 3:9Afi 2:2
1 Ates. 3:102Ti 1:3
1 Ates. 3:102At 1:3; Yuda 20
1 Ates. 3:112At 2:16
1 Ates. 3:122At 1:3
1 Ates. 3:121At 4:9; 2Pe 1:7
1 Ates. 3:131Ak 1:8; Afi 1:10
1 Ates. 3:13Yak 5:8; 1Yo 2:28
1 Ates. 3:131At 2:19; 5:23; 2At 2:1
  • Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Werengani mu Baibulo la Dziko Latsopano (nwt)
  • 1
  • 2
  • 3
  • 4
  • 5
  • 6
  • 7
  • 8
  • 9
  • 10
  • 11
  • 12
  • 13
Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
1 Atesalonika 3:1-13

1 Atesalonika

3 Choncho pamene sitinathenso kupirira, tinaona kuti ndi bwino tingotsala tokha ku Atene.+ 2 Chotero tinatumiza Timoteyo+ m’bale wathu ndi mtumiki wa Mulungu pa uthenga wabwino+ wonena za Khristu, kuti adzakulimbitseni ndi kukutonthozani pa chikhulupiriro chanu, 3 kuti pasapezeke wina wopatutsidwa ndi masautso+ amenewa. Pakuti inu nomwenso mukudziwa kuti tinayeneradi kukumana ndi zimenezi.+ 4 Ndiponso pamene tinali nanu limodzi, tinali kukuuziranitu+ kuti tiyenera kudzakumana ndi masautso,+ ndipo mmene zachitikiramu ndi mmenenso inu mukudziwira.+ 5 Ndiye chifukwa chake pamene sindinathenso kupirira, ndinamutuma kuti ndidziwe za kukhulupirika+ kwanu, kuti mwina mwa njira ina, Woyesayo+ angakhale atakuyesani, ndipo ntchito imene tinagwira mwakhama ingakhale itapita pachabe.+

6 Koma Timoteyo wangofika kumene kwa ife kuchokera kwa inu+ ndipo watiuza nkhani yabwino ya kukhulupirika kwanu ndi chikondi+ chanu. Akuti mukupitiriza kutikumbukira nthawi zonse, ndiponso mukulakalaka kutiona, monganso mmene ife tikulakalakiradi kukuonani.+ 7 Ndiye chifukwa chake abale, mwa kukhulupirika kumene mukusonyeza,+ mwatilimbikitsa+ m’kusowa kwathu konse ndi m’masautso athu onse. 8 Ndipo ife tsopano tilidi ndi moyo chifukwa inu mukukhala olimba mwa Ambuye.+ 9 Kodi Mulungu tingamuyamike bwanji pa nkhani ya inuyo, kuti timubwezere chifukwa cha chimwemwe+ chonse chimene tili nacho chifukwa cha inuyo pamaso pa Mulungu wathu? 10 Komanso usiku ndi usana timapereka mapembedzero amphamvu+ kuti tidzaone nkhope zanu ndi kukwaniritsa zimene zikusowa pa chikhulupiriro chanu.+

11 Tsopano Mulungu wathu ndi Atate mwiniyo, ndi Ambuye wathu Yesu,+ atitsogolere pa ulendo wathu wobwera kwa inu kuti zonse ziyende bwino. 12 Komanso, Ambuye akuthandizeni kuti muwonjezereke,+ ndiponso kuti chikondi+ chanu kwa okhulupirira anzanu ndi kwa ena onse chikule. 13 Achite zimenezi mpaka atalimbitsa mitima yanu ndi kukupangitsani kukhala opanda cholakwa+ ndi oyera pamaso pa Mulungu wathu ndi Atate, pa nthawi ya kukhalapo*+ kwa Ambuye wathu Yesu, limodzi ndi oyera ake onse.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena