Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 52:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Munthu wamphamvu wotere sadalira Mulungu monga malo ake achitetezo,+

      Koma amadalira kuchuluka kwa chuma chake,+

      Ndipo chitetezo chake amachipeza m’mavuto amene iyeyo amawachititsa.+

  • Yesaya 47:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Iwe unali kudalira zoipa zako.+ Wanena kuti: “Palibe amene akundiona.”+ Wasochera chifukwa cha nzeru zako ndiponso chifukwa chodziwa zinthu.+ Mumtima mwako umakhalira kunena kuti: “Ndine ndekha, palibenso wina.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena