Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 41:18-21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Ndiyeno ndinaona ngʼombe 7 zonenepa ndi zooneka bwino zikutuluka mumtsinje wa Nailo, ndipo zinayamba kudya udzu wa mʼmbali mwa mtsinjewo.+ 19 Pambuyo pake ndinaonanso ngʼombe zina 7 zikutuluka mumtsinjewo. Ngʼombe zimenezi zinali zonyansa ndi zowonda. Sindinaonepo ngʼombe zonyansa ngati zimenezo mʼdziko lonse la Iguputo. 20 Ngʼombe zowonda ndi zonyansazo zinayamba kudya ngʼombe 7 zonenepa zija. 21 Koma ngakhale zinadya zinzakezo, palibe akanadziwa chifukwa ngʼombezo zimaonekabe zowonda ngati poyamba. Kenako ndinadzidzimuka.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena