Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 41:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Mʼmawa kutacha, Farao anavutika kwambiri maganizo. Choncho anaitanitsa ansembe onse amatsenga ndi amuna anzeru onse a mu Iguputo, nʼkuwafotokozera malotowo. Koma palibe amene anatha kumumasulira Farao maloto akewo.

  • Danieli 2:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Choncho mfumuyo inalamula kuti aitane ansembe onse ochita zamatsenga, anthu olankhula ndi mizimu, Akasidi* ndi anthu ena ochita zamatsenga kuti adzauze mfumu maloto akewo. Anthu amenewa anafika nʼkuima pamaso pa mfumu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena