Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 45:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Bwererani kwa bambo anga msanga, ndipo mukawauze kuti, ‘Mwana wanu Yosefe wanena kuti: “Mulungu wandiika ine kukhala mbuye wa dziko lonse la Iguputo.+ Bwerani kuno kwa ine, musachedwe.+

  • Genesis 45:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Kumeneko ndizidzakupatsani chakudya chifukwa kwatsala zaka 5 za njala.+ Mukapanda kuchita zimenezi, inuyo ndi amʼnyumba yanu komanso zonse zimene muli nazo muvutika ndi njala.”’

  • Genesis 47:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Chakudya chinatheratu mʼdziko lonselo ndipo njala inafika poipa kwambiri. Anthu onse a ku Iguputo ndi a ku Kanani anali ofooka chifukwa cha njalayo.+

  • Genesis 47:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Tiferenji ife inu mukuona, ndipo minda yathu ikhalirenji yogonera? Mutigule limodzi ndi minda yathu potipatsa chakudya kuti tikhale akapolo a Farao. Mutipatse tirigu kuti tikhale ndi moyo tisafe, komanso kuti minda yathu isagonere.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena