Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 44:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Tsopano Yuda anayandikira kwa Yosefe nʼkunena kuti: “Chonde mbuyanga, ndikukupemphani. Ndiloleni kapolo wanune kuti ndinene mawu amodzi okha. Chonde musandipsere mtima, chifukwa inu muli ngati Farao yemwe.+

  • Genesis 45:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Choncho si inu amene munanditumiza kuno, koma ndi Mulungu woona. Anachita zimenezi kuti andiike kukhala nduna yaikulu ya* Farao, mbuye wa nyumba yake yonse ndiponso wolamulira wa dziko lonse la Iguputo.+

  • Machitidwe 7:9, 10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Mitu ya mabanjayo inachitira nsanje Yosefe+ nʼkumugulitsa ku Iguputo.+ Koma Mulungu anali naye,+ 10 ndipo anamupulumutsa mʼmavuto ake onse. Komanso ankamukonda ndipo ankamuthandiza kuti azichita zinthu mwanzeru pamaso pa Farao mfumu ya Iguputo. Faraoyo anapatsa Yosefe udindo woti aziyangʼanira Iguputo ndi nyumba yake yonse.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena