Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 42:34
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 34 Mukabweretse mʼbale wanu wamngʼonoyo kwa ine kuti ndidzatsimikize kuti si inu akazitape koma anthu achilungamo. Mukatero, ndidzakubwezerani mʼbale wanuyu, ndipo mudzatha kuchita malonda mʼdziko lino.’”

  • Genesis 43:29
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 29 Yosefe atakweza maso ake nʼkuona mngʼono wake Benjamini, mʼbale wake wa mimba imodzi,+ anati: “Kodi uyu ndi mngʼono wanu amene munkanena uja?”+ Ananenanso kuti: “Mulungu akukomere mtima mwana wanga.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena