Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 35:18, 19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Pa nthawi imene moyo wake unkachoka (chifukwa anali akumwalira), anapereka dzina kwa mwanayo lakuti Beni-oni.* Koma bambo ake anamupatsa dzina lakuti Benjamini.*+ 19 Choncho Rakele anamwalira, ndipo anamuika mʼmanda mʼmbali mwa njira yopita ku Efurata, komwe ndi ku Betelehemu.+

  • Genesis 42:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Koma Yakobo sanalole kuti Benjamini,+ mʼbale wake wa Yosefe, apite limodzi ndi abale akewo chifukwa anati: “Mwina ngozi yoopsa ingamuchitikire nʼkufa.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena