Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 43:8, 9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Kenako Yuda anauza Isiraeli bambo ake kuti: “Ndiloleni ndimutenge mnyamatayu+ kuti tinyamuke tizipita kuti tikhalebe ndi moyo tisafe,+ inuyo ndi ife, limodzi ndi ana athuwa.+ 9 Moyo wa mnyamatayu ukhale mʼmanja mwanga.*+ Ngati chinachake chitamuchitikira mudzandilange. Ndikadzapanda kubwera naye ndi kumʼpereka kwa inu, ndidzakhale wochimwa kwa inu moyo wanga wonse.

  • Genesis 44:32
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 32 Ine kapolo wanu ndinalonjeza bambo anga kuti moyo wa mwanayu udzakhala mʼmanja mwanga. Ndinalonjeza kuti, ‘Ndikadzalephera kubwera naye kwa inu, ndidzakhale wochimwa kwa inu bambo anga moyo wanga wonse.’+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena