Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 25:23-28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Mupangenso tebulo+ la mtengo wa mthethe, masentimita 90 mulitali, masentimita 45 mulifupi ndi masentimita 70 kuchoka pansi mpaka mʼmwamba.+ 24 Mudzalikute ndi golide woyenga bwino, ndipo mudzapange mkombero wagolide kuzungulira tebulo lonselo. 25 Mupange felemu kuzungulira tebulo lonse, muyezo wake masentimita 7* mulifupi mwake ndipo mupangenso mkombero wagolide pafelemulo. 26 Tebulolo mulipangire mphete 4 zagolide ndi kuziika mʼmakona ake 4 mmene muli miyendo yake 4. 27 Mphetezo zikhale pafupi ndi felemu kuti muzilowa ndodo zonyamulira tebulolo. 28 Mupangenso ndodo zonyamulira za mtengo wa mthethe ndipo muzikute ndi golide. Ndodo zimenezi azinyamulira tebulolo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena