Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 14:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Ndiyeno Yehova analankhula ndi Mose kuti: “Kodi anthu awa apitiriza kundinyoza mpaka liti?+ Kodi adzayamba liti kundikhulupirira pambuyo pa zizindikiro zonse zimene ndachita pakati pawo?+

  • Salimo 78:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Iwo sanasunge pangano la Mulungu,+

      Ndipo anakana kutsatira chilamulo chake.+

  • Salimo 106:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Koma mofulumira anaiwala zimene Mulungu anachita.+

      Sanadikire kuti Mulungu awapatse malangizo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena