Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yoswa 23:12, 13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Koma mukasiya Mulungu nʼkumamatira anthu a mitundu ina, amene atsala pakati panuwa+ nʼkumakwatirana nawo+ komanso kumagwirizana nawo, 13 dziwani kuti Yehova Mulungu wanu adzasiya kuwathamangitsa pamaso panu.+ Iwo adzakhala ngati msampha ndiponso ngati khwekhwe kwa inu. Adzakhalanso ngati zikwapu kumsana kwanu+ komanso ngati zitsotso mʼmaso mwanu, mpaka mutatheratu mʼdziko labwino limene Yehova Mulungu wanu wakupatsanili.

  • Oweruza 1:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Aisiraeli atakhala amphamvu, anayamba kuwagwiritsa ntchito yaukapolo Akananiwo,+ koma sanawachotseretu onse mʼdzikolo.+

  • Salimo 106:36
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 36 Ankatumikira mafano awo,+

      Ndipo mafanowo anakhala msampha kwa iwo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena