Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 29:45
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 45 Ndidzakhala pakati pa Aisiraeli ndipo ndidzakhala Mulungu wawo.+

  • 1 Mafumu 6:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Komanso ndidzakhala pakati pa Aisiraeli+ ndipo sindidzasiya Aisiraeli, omwe ndi anthu anga.”+

  • Aheberi 9:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Komabe, pamene Khristu anabwera monga mkulu wa ansembe wa zinthu zabwino zimene zakwaniritsidwa, anadzera mʼchihema chachikulu ndi changwiro kwambiri chimene sichinapangidwe ndi manja a anthu, kutanthauza kuti sichipezeka padzikoli.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena