Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mafumu 8:64
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 64 Tsiku limenelo, mfumu inapatula pakati pa bwalo la nyumba ya Yehova chifukwa inkafunika kuperekerapo nsembe zopsereza, nsembe zambewu komanso mafuta a nsembe zamgwirizano. Inachita zimenezi chifukwa guwa lansembe lakopa*+ lapatsogolo pa kachisi wa Yehova linali lalingʼono kwambiri moti nsembe zopsereza, nsembe zambewu ndiponso mafuta+ a nsembe zamgwirizano sizikanakwanapo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena