Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 19:12, 13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Anthuwo uwaikire malire kuzungulira phiri lonse nʼkuwauza kuti, ‘Samalani kuti musakwere mʼphiri kapena kukhudza mʼmunsi mwake. Aliyense wokhudza phirili adzaphedwa ndithu. 13 Munthu aliyense asadzakhudze wolakwayo, koma adzaponyedwe miyala kapena kulasidwa.* Kaya ndi nyama kapena munthu, adzaphedwa.’+ Koma lipenga la nyanga ya nkhosa likadzalira,+ anthu onse adzayandikire phirilo.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena