Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 23:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Muzibweretsa kunyumba ya Yehova Mulungu wanu zipatso zoyamba kucha zamʼminda yanu zomwe ndi zabwino kwambiri.+

      Musamawiritse mwana wa mbuzi mumkaka wa mayi ake.+

  • Numeri 15:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Muzikapereka mikate yozungulira yoboola pakati ya ufa wamisere kuti ikhale chopereka cha zipatso zoyambirira kucha.+ Muzikaipereka ngati mmene mumaperekera chopereka chochokera popunthira mbewu.

  • 2 Mbiri 31:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Aisiraeli atangomva zimenezi, anapereka zinthu zambiri zoyambirira kukolola monga mbewu, vinyo watsopano, mafuta,+ uchi ndi zokolola zonse zakumunda+ ndipo anapereka mowolowa manja chakhumi cha zinthu zonse.+

  • Miyambo 3:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Uzilemekeza Yehova ndi zinthu zako zamtengo wapatali+

      Ndiponso ndi zipatso zako zonse zoyambirira.*+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena