Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 53:5, 6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Koma iye anabayidwa+ chifukwa cha zolakwa zathu.+

      Anaphwanyidwa chifukwa cha zochimwa zathu.+

      Analandira chilango kuti ife tikhale pamtendere,+

      Ndipo chifukwa cha mabala ake ifeyo tinachiritsidwa.+

       6 Tonsefe tikungoyendayenda uku ndi uku ngati nkhosa zosochera.+

      Aliyense akulowera njira yake

      Ndipo Yehova wachititsa kuti zolakwa za tonsefe zigwere pa ameneyo.+

  • 2 Akorinto 5:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Amene analibe uchimoyo,+ Mulungu anamuchititsa kukhala uchimo* chifukwa cha ife, kuti kudzera mwa iye Mulungu azitiona kuti ndife olungama.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena