Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 9:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Koma ngati munthu si wodetsedwa kapena sanali pa ulendo, ndipo wanyalanyaza kukonza nsembe ya Pasika, munthuyo aziphedwa kuti asakhalenso pakati pa anthu ake,+ chifukwa sanapereke nsembeyo kwa Yehova pa nthawi imene inaikidwiratu. Munthuyo adzafa chifukwa cha tchimo lake.

  • Numeri 15:30
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 30 Koma munthu amene wachita tchimo mwadala,+ kaya akhale nzika kapena mlendo, ndiye kuti wanyoza Yehova ndipo ayenera kuphedwa kuti asakhalenso pakati pa anthu ake.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena