Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 29:38
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 38 Zimene uzipereka paguwa lansembelo ndi izi: ana a nkhosa a chaka chimodzi, awiri pa tsiku ndipo uzichita zimenezi nthawi zonse.+

  • Levitiko 6:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 “Lamula Aroni ndi ana ake kuti, ‘Ili ndi lamulo la nsembe yopsereza:+ Nsembe yopsereza izikhala pamoto, paguwa lansembe, usiku wonse mpaka mʼmawa ndipo moto wapaguwapo uzikhala ukuyaka nthawi zonse.

  • Ezekieli 46:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Mʼmawa uliwonse, iwo azipereka kwa ansembe mwana wa nkhosa wamphongo, nsembe yambewu komanso mafuta, kuti zikhale nsembe yopsereza yathunthu ya nthawi zonse.’

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena