Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 20:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Mʼmwezi woyamba, gulu lonse la Aisiraeli linafika mʼchipululu cha Zini, ndipo anthuwo anakhala ku Kadesi.+ Kumeneko nʼkumene Miriamu+ anafera nʼkuikidwa mʼmanda.

  • Numeri 27:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 chifukwa pamene gulu lija linakangana nane mʼchipululu cha Zini, inu munapandukira mawu anga ndipo munalephera kundilemekeza pamaso pa gululo pamadzi+ a Meriba+ ku Kadesi,+ mʼchipululu cha Zini.”+

  • Deuteronomo 32:51
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 51 Izi zili choncho chifukwa awirinu simunakhale okhulupirika kwa ine pakati pa Aisiraeli kumadzi a pa Meriba+ ku Kadesi, mʼchipululu cha Zini, chifukwa simunandilemekeze pamaso pa Aisiraeli.+

  • Yoswa 15:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Gawo limene linaperekedwa+ ku fuko la Yuda kuti ligawidwe kwa mabanja awo linkafika kumalire a Edomu+ ndi kuchipululu cha Zini, mpaka kumapeto kwa Negebu, kumʼmwera.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena