Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 14:38
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 38 Koma Yoswa mwana wa Nuni ndi Kalebe mwana wa Yefune, amene anali mʼgulu la anthu amene anakazonda dziko, adzakhalabe ndi moyo ndithu.”’”+

  • Numeri 27:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Choncho Yehova anauza Mose kuti: “Tenga Yoswa mwana wa Nuni, munthu wolimba mtima,* ndipo uike dzanja lako pa iye.+

  • Yoswa 19:51
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 51 Zimenezi zinali zigawo za cholowa chimene wansembe Eliezara, Yoswa mwana wa Nuni ndi atsogoleri a mafuko a Isiraeli anagawira anthu.+ Anagawa dzikolo pochita maere ku Silo+ pamaso pa Yehova, pakhomo la chihema chokumanako.+ Choncho anamaliza kugawa dzikolo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena