Levitiko 10:9 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 9 “Mukamabwera kuchihema chokumanako, iwe ndi ana ako musamamwe vinyo kapena zakumwa zina zoledzeretsa,+ kuti mungafe. Limeneli ndi lamulo ku mibadwo yanu yonse mpaka kalekale. Amosi 2:11, 12 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 11 Ndinachititsa ana anu ena kukhala aneneri.+Ndipo anyamata anu ena ndinawachititsa kukhala Anaziri.+ Si choncho kodi, inu Aisiraeli?’ watero Yehova. 12 ‘Koma inu munkapatsa Anaziri vinyo kuti amwe,+Ndipo aneneri munawalamula kuti: “Musamanenere.”+ Luka 1:15 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 15 chifukwa adzakhala wamkulu pamaso pa Yehova.*+ Koma asadzamwe vinyo ngakhale pangʼono kapena chakumwa chilichonse choledzeretsa+ ndipo adzadzazidwa ndi mzimu woyera asanabadwe nʼkomwe.*+
9 “Mukamabwera kuchihema chokumanako, iwe ndi ana ako musamamwe vinyo kapena zakumwa zina zoledzeretsa,+ kuti mungafe. Limeneli ndi lamulo ku mibadwo yanu yonse mpaka kalekale.
11 Ndinachititsa ana anu ena kukhala aneneri.+Ndipo anyamata anu ena ndinawachititsa kukhala Anaziri.+ Si choncho kodi, inu Aisiraeli?’ watero Yehova. 12 ‘Koma inu munkapatsa Anaziri vinyo kuti amwe,+Ndipo aneneri munawalamula kuti: “Musamanenere.”+
15 chifukwa adzakhala wamkulu pamaso pa Yehova.*+ Koma asadzamwe vinyo ngakhale pangʼono kapena chakumwa chilichonse choledzeretsa+ ndipo adzadzazidwa ndi mzimu woyera asanabadwe nʼkomwe.*+