Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 29:23, 24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Mʼdengu la mikate yosafufumitsa limene lili pamaso pa Yehova utengemo mkate wobulungira, mkate wozungulira woboola pakati wothira mafuta ndi mkate wopyapyala. 24 Zonsezi uziike mʼmanja mwa Aroni ndi mʼmanja mwa ana ake, ndipo uziyendetse uku ndi uku monga nsembe yoperekedwa kwa Yehova.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena