Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 12:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Kenako anthuwo anachoka ku Hazeroti,+ nʼkukamanga msasa mʼchipululu cha Parana.+

  • Numeri 13:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Iwo anabwerera kwa Mose ndi Aroni ndiponso gulu lonse la Aisiraeli mʼchipululu cha Parana, ku Kadesi.+ Anafotokozera gulu lonselo za ulendo wawo nʼkuwaonetsa zipatso za kudzikolo.

  • Deuteronomo 1:1, 2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 1 Awa ndi mawu amene Mose analankhula ndi Aisiraeli onse mʼchipululu, mʼchigawo cha Yorodano, mʼchigwa chimene chinali moyangʼanizana ndi Sufu, pakati pa Parana, Tofeli, Labani, Hazeroti ndi Dizahabi. 2 Kuchokera ku Horebe kupita ku Kadesi-barinea+ kudzera njira yakuphiri la Seiri pali mtunda woyenda masiku 11.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena