Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 16:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Aisiraeli ataona tinthu timeneti anayamba kufunsana kuti: “Nʼchiyani ichi?” chifukwa sankadziwa kuti chinali chiyani. Mose anawauza kuti: “Ndi chakudya chimene Yehova wakupatsani.+

  • Numeri 11:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Koma pano tilibe ndi mphamvu zomwe. Sitikuonanso chilichonse kupatulapo manawa.”+

  • Salimo 78:24, 25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Iye anapitiriza kuwagwetsera mana ngati mvula kuti adye.

      Anawapatsa tirigu wochokera kumwamba.+

      25 Anthu anadya chakudya cha amphamvu.*+

      Iye anawapatsa chakudya chokwanira.+

Mabuku a Chichewa (1974-2026)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena