Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Levitiko 19:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Komanso, musamakolole mphesa zotsala zamʼmunda mwanu kapena kutola mphesa zimene zamwazika mʼmunda mwanu. Zimenezo muzisiyira anthu osauka*+ ndi mlendo wokhala pakati panu. Ine ndine Yehova Mulungu wanu.

  • Deuteronomo 24:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Musamabere mwachinyengo waganyu yemwe ndi wovutika ndiponso wosauka, kaya akhale mmodzi wa abale anu kapena mlendo amene akukhala mʼdziko lanu, amene ali mʼmizinda yanu.*+

  • Salimo 146:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Yehova akuteteza alendo amene akukhala mʼdziko la eni.

      Amathandiza mwana wamasiye komanso mkazi wamasiye.+

      Koma amasokoneza mapulani a anthu oipa.*+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena