Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 31:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Ngati ndikudalira golide,

      Kapena kuuza golide woyenga bwino kuti, ‘Ndimadalira iwe.’+

  • Yobu 31:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Chimenecho chikanakhala cholakwa chimene oweruza akuyenera kundipatsira chilango,

      Chifukwa ndikanakhala nditakana Mulungu woona wakumwamba.

  • 1 Timoteyo 6:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Koma anthu ofunitsitsa kulemera amakumana ndi mayesero ndiponso amakodwa mumsampha.+ Iwo amalakalaka zinthu zowapweteketsa komanso amachita zinthu mopanda nzeru. Zimenezi zimawawononga ndiponso kuwabweretsera mavuto.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena