-
Yeremiya 32:35Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
35 Kuwonjezera pamenepo, anamangira Baala malo okwera mʼChigwa cha Mwana wa Hinomu*+ kuti aziwotcha* ana awo aamuna ndi ana awo aakazi pamoto ngati nsembe kwa Moleki.+ Ine sindinawalamule+ kuti azichita zimenezi. Ndipo sindinaganizirepo mumtima mwanga* zowauza kuti achite chinthu chonyansa chimenechi, chimene chachititsa kuti Yuda achimwe.’
-