Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Amosi 5:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Chifukwa chakuti mumalamula anthu osauka kuti akulipireni akabwereka munda,

      Ndipo mumatenga zokolola zawo ngati msonkho,+

      Simudzapitiriza kukhala mʼnyumba zamiyala yosema zimene mwamanga.+

      Ndiponso simudzamwa vinyo wochokera mʼminda yanu ya mpesa yabwino kwambiri.+

  • Mika 6:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Mudzadzala mbewu, koma simudzakolola.

      Mudzaponda maolivi, koma simudzagwiritsa ntchito mafuta ake.

      Mudzapanga vinyo watsopano, koma simudzamwa vinyo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena