Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mbiri 36:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Choncho anawabweretsera mfumu ya Akasidi+ yomwe inapha anyamata awo ndi lupanga+ mʼnyumba yopatulika.+ Sinamvere chisoni mnyamata kapena namwali, wachikulire kapena wodwala.+ Mulungu anapereka zonse mʼmanja mwake.+

  • Yesaya 47:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Ine ndinakwiyira anthu anga.+

      Ndinalola kuti cholowa changa chidetsedwe+

      Ndipo ndinawapereka mʼmanja mwako.+

      Koma iwe sunawachitire chifundo.+

      Ngakhale munthu wokalamba unamusenzetsa goli lolemera kwambiri.+

  • Luka 19:44
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 44 Iwo adzakugwetsa pansi nʼkukuwononga limodzi ndi ana ako amene ali mwa iwe.+ Ndipo sadzasiya mwala pamwamba pa mwala unzake mwa iwe,+ chifukwa sunazindikire kuti nthawi yokuyendera inali itakwana.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena