Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 14:44, 45
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 44 Komabe anthuwo anadzikuza ndipo ananyamuka nʼkupita kudera lamapiri kuja,+ koma Mose limodzi ndi likasa la pangano la Yehova sanachoke pakati pa msasa.+ 45 Zitatero Aamaleki ndi Akanani omwe ankakhala kudera lamapirilo anatsika nʼkuyamba kuwapha ndi kuwabalalitsa mpaka ku Horima.+

  • Yoswa 19:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Maere achiwiri+ anagwera Simiyoni, kutanthauza fuko la Simiyoni,+ motsatira mabanja awo. Cholowa chawo chinali pakati pa cholowa cha Yuda.+

  • Yoswa 19:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Elitoladi,+ Betuli, Horima,

  • Oweruza 1:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Koma fuko la Yuda linayendabe ndi abale awo a fuko la Simiyoni, ndipo anapha Akanani okhala ku Zefati nʼkuwononga mzindawo.+ Choncho mzindawo anaupatsa dzina loti Horima.*+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena