Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 15:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Yehova adzalamulira monga mfumu mpaka kalekale.+

  • 1 Samueli 10:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Koma lero mwakana Mulungu wanu+ amene anakupulumutsani mʼmasautso anu onse ndiponso mʼmavuto anu, ndipo munanena kuti: “Ayi, mutisankhire mfumu yoti izitilamulira.” Tsopano imani pamaso pa Yehova potengera mafuko anu ndiponso mabanja anu.’”*

  • Yesaya 33:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Chifukwa Yehova ndi Woweruza wathu,+

      Yehova ndi Wotipatsa Malamulo,+

      Yehova ndi Mfumu yathu.+

      Iye ndi amene adzatipulumutse.+

  • Yesaya 43:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Ine ndine Yehova, Woyera wanu,+ Mlengi wa Isiraeli+ ndiponso Mfumu yanu.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena