Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 36:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Timina anali mkazi wamngʼono wa Elifazi mwana wa Esau. Patapita nthawi, Timina anaberekera Elifazi mwana wamwamuna dzina lake Amaleki.+ Ana a Ada mkazi wa Esau anali amenewa.

  • Ekisodo 17:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 ndipo anati: “Yehova adzamenya nkhondo ndi Aamaleki ku mibadwomibadwo+ chifukwa dzanja lawo laukira mpando wachifumu wa Ya.”+

  • Numeri 13:29
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 29 Aamaleki+ akukhala ku Negebu.+ Ahiti, Ayebusi+ ndi Aamori+ akukhala kudera lamapiri. Akanani+ akukhala mʼmphepete mwa nyanja+ ndi mʼmphepete mwa mtsinje wa Yorodano.”

  • 1 Samueli 15:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Yehova wa magulu ankhondo akumwamba wanena kuti, ‘Ndibwezera Aamaleki chifukwa cha zimene anachitira Aisiraeli polimbana nawo pamene Aisiraeliwo ankachokera ku Iguputo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena