1 Samueli 19:18 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 18 Davide anathawa nʼkukafika kwa Samueli ku Rama+ ndipo anafotokozera Samueli zonse zimene Sauli anamuchitira. Kenako Davide ndi Samueli anachoka nʼkukakhala ku Nayoti.+ 1 Samueli 22:1 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 22 Choncho Davide anachoka kumeneko+ nʼkuthawira kuphanga la Adulamu.+ Azichimwene ake ndi anthu onse amʼnyumba ya bambo ake atamva zimenezi, ananyamuka nʼkumutsatira. 1 Samueli 22:5 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 5 Patapita nthawi, Gadi,+ yemwe anali mneneri, anauza Davide kuti: “Usakhalenso kumalo ovuta kufikako. Chokako kumeneko ndipo upite mʼdziko la Yuda.”+ Choncho Davide anachoka nʼkupita kunkhalango ya Hereti.
18 Davide anathawa nʼkukafika kwa Samueli ku Rama+ ndipo anafotokozera Samueli zonse zimene Sauli anamuchitira. Kenako Davide ndi Samueli anachoka nʼkukakhala ku Nayoti.+
22 Choncho Davide anachoka kumeneko+ nʼkuthawira kuphanga la Adulamu.+ Azichimwene ake ndi anthu onse amʼnyumba ya bambo ake atamva zimenezi, ananyamuka nʼkumutsatira.
5 Patapita nthawi, Gadi,+ yemwe anali mneneri, anauza Davide kuti: “Usakhalenso kumalo ovuta kufikako. Chokako kumeneko ndipo upite mʼdziko la Yuda.”+ Choncho Davide anachoka nʼkupita kunkhalango ya Hereti.