Numeri 24:17 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 17 Ndidzamuona, koma osati panopa;Ndidzamupenya, koma osati posachedwa. Nyenyezi+ idzatuluka mwa Yakobo,Ndodo yachifumu+ idzatuluka mu Isiraeli.+ Ndipo iye adzaphwanyadi chipumi cha Mowabu+Ndi mitu ya asilikali onse ankhanza. Oweruza 3:29 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 29 Pa nthawi imeneyo anapha Amowabu pafupifupi 10,000.+ Onse anali asilikali amphamvu komanso olimba mtima, koma panalibe ngakhale mmodzi amene anapulumuka.+ 1 Samueli 14:47 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 47 Sauli analimbitsa ufumu wake mu Isiraeli ndipo anamenyana ndi adani ake mʼmadera onse. Anamenyana ndi Amowabu,+ Aamoni,+ Aedomu,+ mafumu a Zoba+ ndi Afilisiti.+ Kulikonse kumene ankapita ankagonjetsa adani akewo. Salimo 60:8 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 8 Mowabu ndi beseni langa losambiramo.+ Edomu ndidzamuponyera nsapato zanga.+ Ndidzafuula mosangalala chifukwa chogonjetsa Filisitiya.”+
17 Ndidzamuona, koma osati panopa;Ndidzamupenya, koma osati posachedwa. Nyenyezi+ idzatuluka mwa Yakobo,Ndodo yachifumu+ idzatuluka mu Isiraeli.+ Ndipo iye adzaphwanyadi chipumi cha Mowabu+Ndi mitu ya asilikali onse ankhanza.
29 Pa nthawi imeneyo anapha Amowabu pafupifupi 10,000.+ Onse anali asilikali amphamvu komanso olimba mtima, koma panalibe ngakhale mmodzi amene anapulumuka.+
47 Sauli analimbitsa ufumu wake mu Isiraeli ndipo anamenyana ndi adani ake mʼmadera onse. Anamenyana ndi Amowabu,+ Aamoni,+ Aedomu,+ mafumu a Zoba+ ndi Afilisiti.+ Kulikonse kumene ankapita ankagonjetsa adani akewo.
8 Mowabu ndi beseni langa losambiramo.+ Edomu ndidzamuponyera nsapato zanga.+ Ndidzafuula mosangalala chifukwa chogonjetsa Filisitiya.”+