Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 24:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Ndidzamuona, koma osati panopa;

      Ndidzamupenya, koma osati posachedwa.

      Nyenyezi+ idzatuluka mwa Yakobo,

      Ndodo yachifumu+ idzatuluka mu Isiraeli.+

      Ndipo iye adzaphwanyadi chipumi cha Mowabu+

      Ndi mitu ya asilikali onse ankhanza.

  • 2 Samueli 8:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Davide anagonjetsanso Amowabu+ ndipo anawagoneka pansi nʼkuyamba kuwayeza ndi chingwe. Ankati akayeza zingwe ziwiri, anthu amenewo ankawapha ndipo akayeza chingwe chimodzi, amenewo ankawasiya ndi moyo.+ Amowabuwo anakhala atumiki a Davide ndipo ankapereka msonkho kwa iye.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena