Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 51:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Taonani! Ndinabadwa ndili wochimwa,

      Ndipo ndine wochimwa kuchokera pamene mayi anga anatenga pakati panga.+

  • Salimo 130:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Inu Ya,* mukanakhala kuti mumayangʼanitsitsa* zolakwa,

      Ndi ndani akanaima pamaso panu, inu Yehova?+

  • Mlaliki 7:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Chifukwa padziko lapansi palibe munthu wolungama amene amachita zabwino nthawi zonse ndipo sachimwa.+

  • Aroma 3:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Popeza anthu onse ndi ochimwa ndipo amalephera kusonyeza bwinobwino ulemerero wa Mulungu.+

  • 1 Yohane 1:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Tikamanena kuti, “Tilibe uchimo,” ndiye kuti tikudzinamiza+ ndipo mumtima mwathu mulibe choonadi.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena