Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 12:43
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 43 Kenako Yehova anauza Mose ndi Aroni kuti: “Lamulo la Pasika ndi ili: Mlendo* asadye nawo.+

  • Levitiko 23:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Mʼmwezi woyamba, pa tsiku la 14 la mweziwo,+ madzulo kuli kachisisira,* lizikhala tsiku la Pasika wa Yehova.+

  • Deuteronomo 16:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Ndipo muzipereka nsembe ya Pasika kwa Yehova Mulungu wanu.+ Muzipereka nkhosa ndi ngʼombe+ pamalo amene Yehova adzasankhe kuikapo dzina lake.+

  • 2 Mbiri 35:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 35 Yosiya anachitira Yehova Pasika+ ku Yerusalemu ndipo iwo anapha nyama ya nsembe+ ya Pasika pa tsiku la 14 la mwezi woyamba.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena